Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Chipinda cham’mbali chapansi chinali mikono isanu m’lifupi mwake. Chipinda cham’mbali chapakati chinali mikono 6 m’lifupi mwake, ndipo chipinda cham’mbali chachitatu chinali mikono 7 m’lifupi mwake. Makoma onse akunja a nyumbayo anangowagoba+ n’cholinga choti asawaboole.+

  • 1 Mafumu 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anamanga zipinda zam’mbali+ zosanjikizana kuzungulira nyumba yonseyo. Chipinda chilichonse chinali chotalika mikono isanu. Zipindazo anazilumikiza kunyumbayo ndi matabwa+ a mkungudza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena