Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 41:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kumadzulo kwa nyumbayo kunalinso nyumba ina. Nyumba imeneyo inali mikono 70 m’lifupi mwake. Khoma lonse la nyumbayo linali lochindikala mikono isanu, ndipo m’litali mwake linali mikono 90. Pakati pa nyumba ziwirizi panali mpata waukulu.

  • Ezekieli 41:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Munthu uja anayezanso m’litali mwa nyumba ya kumadzulo ija imene inayang’anizana ndi mpata waukulu. Anayeza timakonde take mbali iyi ndi mbali inayo n’kupeza kuti nyumbayo ndi timakondeto zinali mikono 100.

      Anayezanso kachisi, malo ake amkati+ ndi makonde oyang’ana kubwalo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena