Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 17:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 ndi pamapiri. Katundu wanu ndi chuma chanu chonse ndidzazipereka kuti anthu azifunkhe.+ Ndidzapereka malo anu okwezeka chifukwa cha tchimo limene lachitika m’madera anu onse.+

  • Ezekieli 16:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Ndidzakupereka m’manja mwa anthu okuukira ndipo iwo adzafafaniza mulu wako wadothi+ ndi malo ako okwera.+ Iwo adzakuvula zovala+ ndipo adzatenga zinthu zako zokongola+ n’kukusiya wosavala ndi wamaliseche.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena