Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Uzilemekeza Yehova ndi zinthu zako zamtengo wapatali+ ndiponso ndi zipatso zako zonse zoyambirira.+

  • Ezekieli 48:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anthu inu mupereke gawo lina monga chopereka chanu. Gawolo lichite malire ndi gawo la fuko la Yuda ndipo likhale mikono 25,000 m’lifupi.+ M’litali mwake lifanane ndi magawo a mafuko aja. Malire a gawolo ayambire kum’mawa kukafika kumadzulo. Malo opatulika akhale pakati pa gawo limeneli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena