Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 48:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Malo otsala a mbali iyi ndi mbali inayo ya chopereka chopatulika ndiponso ya mzinda+ akhale a mtsogoleri+ wa anthu. Kumbali ya kum’mawa, malowo achite malire ndi malo operekedwa aja ndipo akhale mikono 25,000 m’lifupi. Kumbali ya kumadzulo, malowo achite malire ndi malo operekedwa aja ndipo akhale mikono 25,000 m’lifupi. Malo a mtsogoleriwo achokere kumbali ya kum’mawa kukafika kumbali ya kumadzulo mofanana ndi magawo a mafuko aja.+ Malo omwe ndi chopereka chopatulika komanso malo opatulika a Nyumba ija akhale pakati pa malo a mtsogoleriwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena