Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 31:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Atamva zimenezo, iye anatenga abale ake n’kuyamba kuthamangira+ Yakobo. Iwo anayenda ulendo wa masiku 7, ndipo anamupeza m’dera la kumapiri la Giliyadi.

  • Numeri 32:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Tsopano ana a Rubeni+ ndi ana a Gadi+ anakhala ndi ziweto zambiri, zankhaninkhani. Iwo anayamba kusirira dziko la Yazeri+ ndi la Giliyadi, ndipo deralo linalidi malo abwino a ziweto.

  • Oweruza 10:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho, amenewa anazunza ndi kupondereza kwambiri ana a Isiraeli chaka chimenecho. Kwa zaka 18, anapondereza ana onse a Isiraeli amene anali kum’mawa kwa Yorodano, m’dziko la Aamori limene linali ku Giliyadi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena