Genesis 48:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Tsopano ana awiri amene unabereka ku Iguputo kuno ine ndisanabwere, ndi ana anga.+ Efuraimu ndi Manase akhala ana anga monga alili Rubeni ndi Simiyoni.+ Yoswa 16:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Malire a kum’mawa a cholowa cha ana a Efuraimu potsata mabanja awo, anali Ataroti-adara+ mpaka kukafika ku Beti-horoni Wakumtunda,+ Yoswa 17:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Poyankha, Yoswa anauza anthu a fuko la Yosefe, omwe ndi Efuraimu ndi Manase, kuti: “Ndinu anthu ochuluka, ndipo ndinu amphamvu kwambiri.+ Simuyenera kukhala ndi gawo limodzi lokha,+
5 Tsopano ana awiri amene unabereka ku Iguputo kuno ine ndisanabwere, ndi ana anga.+ Efuraimu ndi Manase akhala ana anga monga alili Rubeni ndi Simiyoni.+
5 Malire a kum’mawa a cholowa cha ana a Efuraimu potsata mabanja awo, anali Ataroti-adara+ mpaka kukafika ku Beti-horoni Wakumtunda,+
17 Poyankha, Yoswa anauza anthu a fuko la Yosefe, omwe ndi Efuraimu ndi Manase, kuti: “Ndinu anthu ochuluka, ndipo ndinu amphamvu kwambiri.+ Simuyenera kukhala ndi gawo limodzi lokha,+