Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 20:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kenako Pasuri anamenya mneneri Yeremiya+ ndi kumuika m’matangadza+ amene anali pa Chipata Chakumtunda cha Benjamini, cha m’nyumba ya Yehova.

  • Ezekieli 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno ndinaona amuna 6 akubwera kuchokera kuchipata chakumtunda+ choyang’ana kumpoto, aliyense atanyamula chida chake chophwanyira. Pakati pawo panali munthu mmodzi atavala zovala zansalu.+ M’chiuno mwake munali kachikwama ka mlembi, konyamuliramo inki ndi zolembera. Anthuwo analowa mkati n’kuima pambali pa guwa lansembe lamkuwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena