Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Apatuka mofulumira panjira imene ndawalamula kuyendamo.+ Iwo adzipangira fano la mwana wa ng’ombe lopangidwa ndi golide wosungunula. Akuligwadira ndi kupereka nsembe kwa fanolo, ndipo akunena kuti, ‘Aisiraeli inu, uyu ndiye Mulungu wanu amene anakutsogolerani potuluka m’dziko la Iguputo.’”+

  • Numeri 14:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma anthu onse amene aona ulemerero wanga,+ ndi zizindikiro zanga+ zimene ndinachita ku Iguputo, ndi zimene ndachita m’chipululu, amene akupitirizabe kundiyesa+ maulendo 10 onsewa, amenenso sanamvere mawu anga,+

  • Salimo 78:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Iwo analitu kumupandukira kawirikawiri m’chipululu,+

      Anali kumukhumudwitsa m’chipululumo!+

  • Salimo 95:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Musaumitse mitima yanu monga mmene makolo anu anachitira pa Meriba,+

      Monga mmene anachitira pa Masa m’chipululu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena