Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Pa nthawi imeneyo Danieli, wotchedwa Belitesazara,+ anada nkhawa kwa kanthawi ndipo anachita mantha.+

      “Chotero mfumuyo inamuuza kuti, ‘Iwe Belitesazara, malotowa ndi kumasulira kwake zisakuchititse mantha.’+

      “Belitesazara anayankha kuti, ‘Inu mbuyanga, zikanakhala bwino malotowa akanakhala okhudza anthu amene amadana nanu. Zikanakhalanso bwino kumasulira kwake kukanakhala kokhudza adani anu.+

  • Danieli 4:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Nthawi yomweyo+ mawuwa anakwaniritsidwa pa Nebukadinezara ndipo anathamangitsidwa pakati pa anthu. Iye anayamba kudya udzu ngati ng’ombe ndipo thupi lake linkanyowa ndi mame akumwamba. Tsitsi lake linatalika kwambiri ngati nthenga za chiwombankhanga ndipo zikhadabo zake zinatalika ngati za mbalame.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena