Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pa tsiku la nsautso undiitane.+

      Ine ndidzakulanditsa, ndipo iwe udzandilemekeza.”+

  • Miyambo 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Khulupirira Yehova ndi mtima wako wonse,+ ndipo usadalire luso lako lomvetsa zinthu.+

  • Mateyu 18:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ndiponso ndikukuuzani kuti, ngati awiri mwa inu padziko lapansi pano adzagwirizana pa chilichonse chofunika kupempha, Atate wanga wakumwamba adzawachitira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena