2 Mbiri 33:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Iye atasautsika mumtima mwake chifukwa cha zimenezi,+ anakhazikitsa pansi mtima wa Yehova Mulungu wake+ ndipo anadzichepetsa+ kwambiri pamaso pa Mulungu wa makolo ake. Salimo 77:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Pa tsiku la zowawa zanga ndafunafuna Yehova.+Ndakweza dzanja langa kumwamba usiku wonse, ndipo silinachite dzanzi.Koma sindinatonthozeke.+ Salimo 91:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Adzandiitana ndipo ndidzamuyankha.+Ndidzakhala naye m’nthawi ya masautso.+Ndidzamupulumutsa ndi kumupatsa ulemerero.+ Luka 22:44 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 44 Koma atazunzika koopsa mumtima mwake, anapitiriza kupemphera ndi mtima wonse+ ndipo thukuta lake linaoneka ngati madontho amagazi amene akugwera pansi.+
12 Iye atasautsika mumtima mwake chifukwa cha zimenezi,+ anakhazikitsa pansi mtima wa Yehova Mulungu wake+ ndipo anadzichepetsa+ kwambiri pamaso pa Mulungu wa makolo ake.
2 Pa tsiku la zowawa zanga ndafunafuna Yehova.+Ndakweza dzanja langa kumwamba usiku wonse, ndipo silinachite dzanzi.Koma sindinatonthozeke.+
15 Adzandiitana ndipo ndidzamuyankha.+Ndidzakhala naye m’nthawi ya masautso.+Ndidzamupulumutsa ndi kumupatsa ulemerero.+
44 Koma atazunzika koopsa mumtima mwake, anapitiriza kupemphera ndi mtima wonse+ ndipo thukuta lake linaoneka ngati madontho amagazi amene akugwera pansi.+