Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 12:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Anthu onse omuzungulira amene amamuthandiza, ndiponso magulu ake onse ankhondo, ndidzawabalalitsira ku mphepo zonse zinayi,+ ndipo ndidzawatsatira nditasolola lupanga.+

  • Ezekieli 17:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Gulu lonse la asilikali ake amene anathawa, lidzaphedwa ndi lupanga. Amene adzapulumuke adzabalalikira ku mphepo zonse.+ Anthu inu mudzadziwa kuti ine Yehova ndi amene ndanena zimenezi.”’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena