Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 24:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti ndi Yehova Mulungu wathu amene anatitulutsa m’dziko la Iguputo+ pamodzi ndi makolo athu, kutichotsa m’nyumba yaukapolo.+ Iye anachita zizindikiro zazikulu pamaso pathu+ ndi kutiteteza m’njira yonse imene tinayenda, ndiponso kwa mitundu yonse ya anthu amene tinadutsa pakati pawo.+

  • 1 Samueli 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Yakobo atangofika mu Iguputo,+ makolo anu n’kuyamba kupempha thandizo+ kwa Yehova, Yehova anatumiza Mose+ ndi Aroni kuti atsogolere makolo anu potuluka mu Iguputo, ndipo anawapatsa dziko lino kuti akhalemo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena