-
Obadiya 20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Anthu amene anatengedwa kupita kudziko lina kuchokera pachiunda ichi chomenyerapo nkhondo,+ amene ndi ana a Isiraeli, adzatenga zinthu zimene zinali za Akanani+ mpaka kukafika ku Zarefati.+ Anthu amene anatengedwa kuchokera ku Yerusalemu kupita kudziko lina, amene anali ku Sefaradi, adzatenga mizinda ya Negebu kukhala yawo.+
-