Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 24:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Iye anapitiriza kulankhula mawu ake a ndakatulo, kuti:

      “Kalanga ine! Adzapulumuke tsokalo ndani, Mulungu akadzaliponya?+

  • Nahumu 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye atapsa mtima, ndani angaime pamaso pake?+ Iye atakwiya, ndani angalimbe mtima kuima pamaso pake?+

      Mkwiyo wake adzaukhuthula ngati moto+ ndipo miyala idzagwetsedwa chifukwa cha iye.

  • Chivumbulutso 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 chifukwa tsiku lalikulu+ la mkwiyo wawo+ lafika, ndipo ndani angaimirire pamaso pawo?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena