1 Samueli 3:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Zili choncho, mwanayo Samueli anali kutumikira+ Yehova pamaso pa Eli, ndipo mawu a Yehova+ anali osowa masiku amenewo,+ moti masomphenya sanali kuonekaoneka.+ Salimo 74:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Zizindikiro zathu sitinazione, ndipo palibenso mneneri amene watsala,+Pakati pathu palibe amene akudziwa kuti zikhala choncho mpaka liti. Ezekieli 7:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 M’dzikolo mudzakhala mavuto otsatizanatsatizana+ ndipo muzidzamveka mauthenga otsatizanatsatizana. Anthu azidzafunafuna masomphenya kwa mneneri.+ Ansembe sadzathanso kuphunzitsa malamulo aphindu. Anthu achikulire sadzaperekanso malangizo othandiza.+ Mateyu 4:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Koma poyankha iye anati: “Malemba amati, ‘Munthu sangakhale ndi moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mawu onse otuluka pakamwa pa Yehova.’”*+
3 Zili choncho, mwanayo Samueli anali kutumikira+ Yehova pamaso pa Eli, ndipo mawu a Yehova+ anali osowa masiku amenewo,+ moti masomphenya sanali kuonekaoneka.+
9 Zizindikiro zathu sitinazione, ndipo palibenso mneneri amene watsala,+Pakati pathu palibe amene akudziwa kuti zikhala choncho mpaka liti.
26 M’dzikolo mudzakhala mavuto otsatizanatsatizana+ ndipo muzidzamveka mauthenga otsatizanatsatizana. Anthu azidzafunafuna masomphenya kwa mneneri.+ Ansembe sadzathanso kuphunzitsa malamulo aphindu. Anthu achikulire sadzaperekanso malangizo othandiza.+
4 Koma poyankha iye anati: “Malemba amati, ‘Munthu sangakhale ndi moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mawu onse otuluka pakamwa pa Yehova.’”*+