Yesaya 60:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Anthu ako onse adzakhala olungama.+ Iwo adzakhala m’dzikomo mpaka kalekale.+ Anthuwo adzakhala mmera wobzalidwa ndi ine+ ndiponso ntchito ya manja anga,+ kuti ineyo ndikongoletsedwe.+ Yeremiya 24:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Maso anga adzakhala pa iwo kuti ndiwachitire zabwino,+ ndipo ndidzawabwezeretsa kudziko lino.+ Pamenepo ndidzawalimbitsa, osati kuwapasula. Ndidzawabzala, osati kuwazula.+ Ezekieli 34:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Iwo sadzabedwanso ndi anthu a mitundu ina.+ Chilombo chakutchire sichidzawadyanso. Adzakhala mwabata popanda wowaopsa.+ Ezekieli 37:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Anthu amenewa adzakhala m’dziko limene ndinapatsa mtumiki wanga Yakobo, dziko limene makolo anu anakhalamo.+ Adzakhala m’dzikomo+ pamodzi ndi ana awo ndiponso zidzukulu zawo mpaka kalekale.+ Davide mtumiki wanga adzakhala mtsogoleri wawo mpaka kalekale.+ Yoweli 3:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Koma mu Yuda mudzakhala anthu mpaka kalekale,+ ndipo mu Yerusalemu mudzakhala anthu ku mibadwomibadwo.+
21 Anthu ako onse adzakhala olungama.+ Iwo adzakhala m’dzikomo mpaka kalekale.+ Anthuwo adzakhala mmera wobzalidwa ndi ine+ ndiponso ntchito ya manja anga,+ kuti ineyo ndikongoletsedwe.+
6 Maso anga adzakhala pa iwo kuti ndiwachitire zabwino,+ ndipo ndidzawabwezeretsa kudziko lino.+ Pamenepo ndidzawalimbitsa, osati kuwapasula. Ndidzawabzala, osati kuwazula.+
28 Iwo sadzabedwanso ndi anthu a mitundu ina.+ Chilombo chakutchire sichidzawadyanso. Adzakhala mwabata popanda wowaopsa.+
25 Anthu amenewa adzakhala m’dziko limene ndinapatsa mtumiki wanga Yakobo, dziko limene makolo anu anakhalamo.+ Adzakhala m’dzikomo+ pamodzi ndi ana awo ndiponso zidzukulu zawo mpaka kalekale.+ Davide mtumiki wanga adzakhala mtsogoleri wawo mpaka kalekale.+
20 Koma mu Yuda mudzakhala anthu mpaka kalekale,+ ndipo mu Yerusalemu mudzakhala anthu ku mibadwomibadwo.+