Deuteronomo 2:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Sihoni atatuluka pamodzi ndi anthu ake onse kudzamenyana nafe nkhondo ku Yahazi,+ Deuteronomo 2:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Yehova Mulungu wathu anam’pereka kwa ife,+ ndipo tinam’gonjetsa+ limodzi ndi ana ake ndi anthu ake onse.
33 Yehova Mulungu wathu anam’pereka kwa ife,+ ndipo tinam’gonjetsa+ limodzi ndi ana ake ndi anthu ake onse.