Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 103:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yehova wakhazikitsa mpando wake wachifumu kumwamba.+

      Ndipo ufumu wake ukulamulira chilichonse.+

  • Salimo 115:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kunena za kumwamba, kumwamba ndi kwa Yehova,+

      Koma dziko lapansi analipereka kwa ana a anthu.+

  • Salimo 136:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yamikani Mulungu wakumwamba:+

      Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena