Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 106:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chotero anawapulumutsa m’manja mwa wodana nawo,+

      Ndipo anawawombola m’manja mwa mdani.+

  • Salimo 107:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Anthu owomboledwa a Yehova anene zimenezi,+

      Anthu amene iye wawawombola m’manja mwa mdani,+

  • Yesaya 48:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tulukani m’Babulo anthu inu!+ Thawani m’manja mwa Akasidi.+ Nenani zimenezi ndi mfuu yachisangalalo kuti zimveke.+ Zineneni mokuwa mpaka zimveke kumalekezero a dziko lapansi.+ Munene kuti: “Yehova wawombola mtumiki wake Yakobo.+

  • Yeremiya 15:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Ndidzakulanditsa m’manja mwa anthu oipa+ ndipo ndidzakuwombola m’manja mwa anthu ankhanza.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena