Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ena akunena za magaleta* ndipo ena akunena za mahatchi,*+

      Koma ife tidzanena za dzina la Yehova Mulungu wathu.+

  • Salimo 33:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Palibe mfumu imene inapulumuka chifukwa cha kukula kwa gulu lake lankhondo.+

      Munthu wamphamvu sapulumuka chifukwa cha kuchuluka kwa mphamvu zake.+

  • Hoseya 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma ndidzachitira chifundo nyumba ya Yuda,+ ndipo Ine Yehova Mulungu wawo, ndidzawapulumutsa.+ Sindidzawapulumutsa ndi uta, lupanga, nkhondo, mahatchi* kapena ndi amuna okwera pamahatchi ayi.”+

  • Hoseya 14:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Dziko la Asuri silidzatipulumutsa.+ Ife sitidzakwera pamahatchi.+ Sitidzauzanso ntchito ya manja athu kuti: “Inu Mulungu wathu!” chifukwa inu mumachitira chifundo mwana wamasiye.’*+

  • Zekariya 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndidzawononga magaleta ankhondo mu Efuraimu ndiponso mahatchi mu Yerusalemu.+ Mauta omenyera nkhondo+ adzathyoledwa. Mfumuyo idzalankhula mawu amtendere kwa anthu a mitundu ina.+ Ulamuliro wake udzayambira kunyanja mpaka kukafika kunyanja. Ndiponso udzachokera ku Mtsinje* mpaka kumalekezero a dziko lapansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena