Numeri 23:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Pamenepo Balamu anayambanso kulankhula mwa ndakatulo, kuti:+“Nyamuka, Balaki iwe, tamvera.Tchera khutu kwa ine, iwe mwana wa Zipori.+ Yobu 27:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Tsopano Yobu anayambanso kulankhula mwandakatulo+ kuti: Habakuku 2:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Kodi anthu onsewa sadzamunenera mwambi,+ chining’a ndi mawu okuluwika? Wina adzanena kuti,“‘Kodi iye adzapitiriza kuchulukitsa zinthu zimene si zake+ kwa nthawi yaitali bwanji?+ Tsoka kwa iye pakuti akungochulukitsa ngongole yake.
18 Pamenepo Balamu anayambanso kulankhula mwa ndakatulo, kuti:+“Nyamuka, Balaki iwe, tamvera.Tchera khutu kwa ine, iwe mwana wa Zipori.+
27 Tsopano Yobu anayambanso kulankhula mwandakatulo+ kuti: Habakuku 2:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Kodi anthu onsewa sadzamunenera mwambi,+ chining’a ndi mawu okuluwika? Wina adzanena kuti,“‘Kodi iye adzapitiriza kuchulukitsa zinthu zimene si zake+ kwa nthawi yaitali bwanji?+ Tsoka kwa iye pakuti akungochulukitsa ngongole yake.
6 Kodi anthu onsewa sadzamunenera mwambi,+ chining’a ndi mawu okuluwika? Wina adzanena kuti,“‘Kodi iye adzapitiriza kuchulukitsa zinthu zimene si zake+ kwa nthawi yaitali bwanji?+ Tsoka kwa iye pakuti akungochulukitsa ngongole yake.