Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Dziko lapansi linayamba kugwedezekera uku ndi uku ndiponso kutekeseka.+

      Maziko a kumwamba anagwedezeka.+

      Anagwedezekera uku ndi uku chifukwa Mulungu anakwiya.+

  • Salimo 68:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Dziko lapansi linagwedezeka,+

      Kumwamba kunagwa mvula chifukwa cha inu Mulungu,+

      Phiri ili la Sinai linagwedezeka chifukwa cha inu Mulungu,+ Mulungu wa Isiraeli.+

  • Salimo 97:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mapiri anasungunuka ngati phula chifukwa cha Yehova,+

      Chifukwa cha Ambuye wa dziko lonse lapansi.+

  • Aheberi 12:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pa nthawiyo, mawu ake anagwedeza dziko lapansi,+ koma tsopano walonjeza kuti: “Ndidzagwedezanso kumwamba, osati dziko lapansi lokhali.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena