Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 20:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 momwemonso mfumu ya Asuri idzagwira gulu la anthu ku Iguputo+ ndi ku Itiyopiya n’kupita nawo ku ukapolo kudziko lina, anyamata ndi nkhalamba, ali opanda zovala ndi opanda nsapato, ndiponso matako awo ali pamtunda. Pamenepo, umaliseche wa Iguputo udzaonekera.+

  • Yeremiya 29:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Awa ndi mawu a m’kalata imene mneneri Yeremiya anatumiza kuchokera ku Yerusalemu kupita kwa akuluakulu otsala pakati pa anthu amene anali ku ukapolo, kwa ansembe ndi kwa aneneri. Kalatayi inapitanso kwa anthu onse amene Nebukadinezara anawatenga kupita nawo ku ukapolo ku Babulo kuchokera ku Yerusalemu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena