2 Samueli 11:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Kuwonjezera apo, Davide anamuitana kuti adye ndi kumwa naye pamodzi, ndipo anamuledzeretsa.+ Ngakhale zinali choncho, madzulo Uriya anapita kwa atumiki a mbuye wake kukagona pabedi, ndipo sanapite kunyumba kwake. 2 Samueli 13:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Kenako Abisalomu analamula omutumikira kuti: “Muonetsetse chonde kuti Aminoni akangosangalala mumtima mwake ndi vinyo,+ ine n’kukuuzani kuti, ‘Mukantheni Aminoni!’ pamenepo mumuphe. Musaope.+ Kodi si ndine amene ndakulamulani? Chitani zinthu mwamphamvu ndipo khalani olimba mtima.” Chivumbulutso 17:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 limene mafumu a dziko lapansi anachita nalo dama,+ ndipo linaledzeretsa anthu okhala padziko lapansi ndi vinyo wa dama* lake.”+ Chivumbulutso 18:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Iye wamwetsa mitundu yonse ya anthu+ vinyo wa mkwiyo, vinyo wa dama lake. Ndipo mafumu a dziko lapansi anachita naye dama.+ Amalonda oyendayenda+ a padziko lapansi analemera chifukwa cha zinthu zambiri zamtengo wapatali zimene mkazi ameneyu anadziunjikira mopanda manyazi.”+
13 Kuwonjezera apo, Davide anamuitana kuti adye ndi kumwa naye pamodzi, ndipo anamuledzeretsa.+ Ngakhale zinali choncho, madzulo Uriya anapita kwa atumiki a mbuye wake kukagona pabedi, ndipo sanapite kunyumba kwake.
28 Kenako Abisalomu analamula omutumikira kuti: “Muonetsetse chonde kuti Aminoni akangosangalala mumtima mwake ndi vinyo,+ ine n’kukuuzani kuti, ‘Mukantheni Aminoni!’ pamenepo mumuphe. Musaope.+ Kodi si ndine amene ndakulamulani? Chitani zinthu mwamphamvu ndipo khalani olimba mtima.”
2 limene mafumu a dziko lapansi anachita nalo dama,+ ndipo linaledzeretsa anthu okhala padziko lapansi ndi vinyo wa dama* lake.”+
3 Iye wamwetsa mitundu yonse ya anthu+ vinyo wa mkwiyo, vinyo wa dama lake. Ndipo mafumu a dziko lapansi anachita naye dama.+ Amalonda oyendayenda+ a padziko lapansi analemera chifukwa cha zinthu zambiri zamtengo wapatali zimene mkazi ameneyu anadziunjikira mopanda manyazi.”+