Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iwe unali mzinda wodzaza ndi chipwirikiti, waphokoso, komanso unali mudzi wokondwa.+ Anthu ako amene aphedwa, sanaphedwe ndi lupanga ndiponso sanaphedwe kunkhondo.+

  • Yesaya 47:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Iwe unali kunena kuti: “Ine ndidzakhala Dona mpaka kalekale,+ mpaka muyaya.” Sunaganizire zinthu izi mumtima mwako ndipo sunaganizire kuti zidzatha bwanji.+

  • Nahumu 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Tsoka mzinda wokhetsa magazi.+ Mzindawo wadzaza ndi chinyengo ndi chifwamba, moti nthawi zonse umafunkha zinthu za anthu ena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena