Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 35:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kumeneko kudzakhala msewu waukulu+ ndipo udzatchedwa Msewu wa Chiyero.+ Munthu wodetsedwa sadzayendamo.+ Amene adzayendemo ndi munthu yekhayo amene ali woyenerera. Palibe anthu opusa amene azidzayendayendamo.

  • Ezekieli 44:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Mlendo aliyense amene ali pakati pa ana a Isiraeli, wosachita mdulidwe wa mtima ndi mdulidwe wa khungu, asalowe m’malo anga opatulika.”’+

  • Chivumbulutso 21:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Koma chilichonse chosapatulika, ndi aliyense wochita zonyansa+ ndiponso wabodza,+ sadzalowa mumzindawo.+ Amene adzalowemo ndi okhawo olembedwa mumpukutu wa moyo, umene ndi wa Mwanawankhosa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena