9 “‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Mlendo aliyense amene ali pakati pa ana a Isiraeli, wosachita mdulidwe wa mtima ndi mdulidwe wa khungu, asalowe m’malo anga opatulika.”’+
27 Koma chilichonse chosapatulika, ndi aliyense wochita zonyansa+ ndiponso wabodza,+ sadzalowa mumzindawo.+ Amene adzalowemo ndi okhawo olembedwa mumpukutu wa moyo, umene ndi wa Mwanawankhosa.+