Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma Mulungu adzauza woipa kuti:+

      “Ndani wakupatsa udindo wofotokoza malangizo anga,+

      Ndi wolankhula za pangano langa?+

  • Yoweli 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamenepo anthu inu mudzadziwa kuti ine ndine Yehova Mulungu wanu,+ amene ndimakhala mu Ziyoni, phiri langa lopatulika.+ Yerusalemu adzakhala malo anga opatulika,+ ndipo alendo sadzadutsanso mmenemo.+

  • Zekariya 14:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mphika uliwonse wakukamwa kwakukulu mu Yerusalemu ndi mu Yuda udzakhala woyera ndipo udzakhala wa Yehova wa makamu. Anthu onse amene azidzapereka nsembe azidzabwera n’kutengako ina mwa miphikayo ndi kuphikiramo.+ Pa tsiku limenelo, m’nyumba ya Yehova wa makamu+ simudzapezeka Mkanani.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena