21 Mphika uliwonse wakukamwa kwakukulu mu Yerusalemu ndi mu Yuda udzakhala woyera ndipo udzakhala wa Yehova wa makamu. Anthu onse amene azidzapereka nsembe azidzabwera n’kutengako ina mwa miphikayo ndi kuphikiramo.+ Pa tsiku limenelo, m’nyumba ya Yehova wa makamu+ simudzapezeka Mkanani.”+