Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 46:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Gonjerani anthu inu, ndipo dziwani kuti ine ndine Mulungu.+

      Ndidzakwezedwa pakati pa anthu a mitundu ina,+

      Ndidzakwezedwa padziko lapansi.”+

  • Habakuku 2:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma Yehova ali m’kachisi wake wopatulika.+ Inu anthu onse a padziko lapansi, khalani chete pamaso pake!’”+

  • Zefaniya 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Khalani chete pamaso pa Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa,+ pakuti tsiku la Yehova lili pafupi,+ ndipo Yehova wakonza nsembe+ moti wakonzekeretsa*+ anthu amene wawaitana.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena