Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova ali m’kachisi wake wopatulika.+

      Yehova, mpando wake wachifumu uli kumwamba.+

      Maso ake amaona, maso ake owala amasanthula+ ana a anthu.

  • Salimo 115:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Koma Mulungu wathu ali kumwamba.+

      Chilichonse chimene anafuna kuchita anachita.+

  • Yesaya 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 M’chaka chimene Mfumu Uziya inamwalira,+ ine ndinaona Yehova+ atakhala pampando wachifumu+ wolemekezeka umene unali pamalo okwezeka, ndipo zovala zake zinadzaza m’kachisi.+

  • Aheberi 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iye ndi wantchito wotumikira ena wa m’malo oyerawo+ komanso m’chihema chenicheni, chomangidwa ndi Yehova,+ osati munthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena