Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ugwiritse ntchito mmisiri wogoba kuti alembe mayina a ana a Isiraeli pamiyala iwiriyo mwaluso la wogoba miyala.+ Awalembe ngati mmene amagobera chidindo. Apange miyalayo moti izitha kulowa m’zoikamo zake zagolide.+

  • Yohane 6:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Musamagwire ntchito kuti mungopeza chakudya chimene chimawonongeka,+ koma kuti mupeze chakudya chokhalitsa, chopereka moyo wosatha,+ chimene Mwana wa munthu adzakupatsani. Pakuti Atate, Mulungu yekhayo, waika chisindikizo pa iye chomuvomereza.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena