Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliro 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zimenezi zinachitika chifukwa cha machimo a aneneri ake ndi zolakwa za ansembe ake,+

      Amene anakhetsa magazi a anthu olungama a mumzindawo.+

  • Hoseya 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Imvani inu ansembe+ ndipo mvetserani inu a m’nyumba ya Isiraeli. Inunso a m’nyumba ya mfumu+ mvetserani, pakuti chiweruzochi chikukhudza inuyo, chifukwa mwakhala msampha+ ku Mizipa ndipo mwakhala ngati ukonde paphiri la Tabori.+

  • Malaki 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “‘Mwana amalemekeza bambo ake+ ndipo wantchito amalemekeza mbuye wake.+ Ngati ine ndili atate,+ ulemu wanga uli kuti?+ Ngati ndili Ambuye Wamkulu, n’chifukwa chiyani simundiopa?’+ watero Yehova wa makamu kwa inu ansembe amene mukunyoza dzina langa.+

      “‘Inu mukunena kuti: “Kodi dzina lanu talinyoza motani?”’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena