Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 41:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Koma munthu amene ndinali kukhala naye mwamtendere, amene ndinali kumukhulupirira,+

      Munthu amene anali kudya chakudya changa,+ wakweza chidendene chake kundiukira.+

  • Maliko 14:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iye anati: “Ndi mmodzi wa inu 12, amene akusunsa nane m’mbale imodzi.+

  • Luka 22:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Koma taonani! Wondipereka+ ndili naye limodzi patebulo pompano.+

  • Yohane 13:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Yesu anayankha kuti: “Ndi amene ndimupatse chidutswa cha mkate chimene ndisunse.”+ Choncho atasunsa chidutswa cha mkate chija, anapatsa Yudasi, mwana wa Simoni Isikariyoti.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena