Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 24:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Aliyense wopanda mlandu m’manja mwake ndi woyera mumtima mwake,+

      Amene sanaone Moyo wanga ngati wopanda pake,+

      Kapena kulumbira mwachinyengo.+

  • Salimo 73:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 73 Mulungu ndi wabwinodi kwa Isiraeli, kwa anthu oyera mtima.+

  • Miyambo 22:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Amene amakondwera kukhala ndi mtima woyera+ ndiponso amene mawu ake ndi okopa, adzakhala bwenzi la mfumu.+

  • Tito 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Zinthu zonse n’zoyera kwa anthu oyera.+ Koma kwa anthu oipitsidwa+ ndi opanda chikhulupiriro+ kulibe choyera, m’malomwake maganizo awo ndi chikumbumtima+ chawo n’zoipa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena