Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 9:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Koma ku Yopa+ kunali wophunzira wina dzina lake Tabita, dzina limene polimasulira limatanthauza Dorika.* Tabita anali kuchita ntchito zabwino zambiri,+ ndi kupereka mphatso zachifundo zochuluka.

  • Machitidwe 10:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iyeyu anali wopembedza+ ndi woopa+ Mulungu pamodzi ndi banja lake lonse. Anali kupatsa anthu mphatso zambiri zachifundo+ ndipo anali kupemphera kwa Mulungu nthawi zonse.+

  • 1 Akorinto 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ngati ndapereka zanga zonse kudyetsa ena,+ ndipo ngati ndapereka thupi langa+ kuti ndidzitame, koma ndilibe chikondi,+ sindinapindule m’pang’ono pomwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena