Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 8:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Koma iye anawafunsa kuti: “N’chifukwa chiyani mukuchita mantha chonchi, anthu achikhulupiriro chochepa inu?”+ Kenako anadzuka n’kudzudzula mphepo ndi nyanjayo, ndipo panachita bata lalikulu.+

  • Mateyu 14:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Nthawi yomweyo Yesu anatambasula dzanja lake ndi kum’gwira dzanja n’kumuuza kuti: “Wachikhulupiriro chochepa iwe, n’chifukwa chiyani wakayikira?”+

  • Mateyu 16:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yesu anadziwa zimenezi ndipo ananena kuti: “Inu achikhulupiriro chochepa, mulibe mikate. Ndiye n’chifukwa chiyani mukukambirana zimenezi?+

  • Luka 12:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsopano ngati Mulungu amaveka chotero zomera zakutchire, zimene zimangokhalapo lero lokha, mawa n’kuzisonkhezera pamoto, kuli bwanji inu, achikhulupiriro chochepa inu! Ndithudi, iye adzakuvekani kuposa pamenepo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena