Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 65:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye akutontholetsa phokoso la nyanja,+

      Akutontholetsa phokoso la mafunde ake komanso chipwirikiti cha mitundu ya anthu.+

  • Salimo 89:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Nyanja ikadzaza mumailamulira.+

      Mafunde ake akamawinduka, inuyo mumawakhalitsa bata.+

  • Salimo 107:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Iye amachititsa mphepo yamkuntho kukhala bata,+

      Moti mafunde a panyanja amadekha.+

  • Luka 8:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndiyeno anawafunsa kuti: “Chikhulupiriro chanu chili kuti?” Koma iwo anagwidwa ndi mantha ndipo anathedwa nzeru, mwakuti anayamba kufunsana kuti: “Kodi ameneyu ndani kwenikweni, wochita kulamula mphepo ndi madzi ndipo n’kumumvera?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena