Maliko 1:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Koma apongozi aakazi a Simoni+ anali chigonere, akudwala malungo.*+ Mwamsanga iwo anamuuza za mayiyo. Luka 4:38 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 38 Atatuluka m’sunagogemo, anakalowa m’nyumba ya Simoni. Kumeneko apongozi aakazi a Simoni anali kudwala malungo* aakulu, choncho anam’pempha kuti apite kumeneko chifukwa cha mayiwo.+
30 Koma apongozi aakazi a Simoni+ anali chigonere, akudwala malungo.*+ Mwamsanga iwo anamuuza za mayiyo.
38 Atatuluka m’sunagogemo, anakalowa m’nyumba ya Simoni. Kumeneko apongozi aakazi a Simoni anali kudwala malungo* aakulu, choncho anam’pempha kuti apite kumeneko chifukwa cha mayiwo.+