41 Anthu a ku Nineve adzaimirira pa chiweruzo limodzi ndi m’badwo uwu+ ndipo adzautsutsa,+ chifukwa iwo analapa atamva ulaliki wa Yona.+ Koma tsopano wina woposa Yona ali pano.
32 Anthu a ku Nineve adzaimirira pa chiweruzo limodzi ndi m’badwo uwu ndipo adzautsutsa. Chifukwa iwo analapa atamva ulaliki wa Yona.+ Koma tsopano wina woposa+ Yona ali pano.