-
Luka 6:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Kenako anatsika nawo ndi kuima pamalo am’munsi, athyathyathya. Pamenepo panali khamu lalikulu la ophunzira ake. Panalinso chikhamu cha anthu+ ochokera ku Yudeya konse ndi ku Yerusalemu konse, komanso kumadera am’mphepete mwa nyanja a ku Turo ndi ku Sidoni. Onsewo anabwera kudzamumvetsera ndi kudzachiritsidwa matenda awo.+
-