Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 13:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Komanso mbewu zina zinagwera paminga, ndipo mingazo zinakula ndi kulepheretsa mbewuzo kukula.+

  • Maliko 4:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno palinso mbewu zina zofesedwa paminga. Zimenezi ndiwo anthu amene amamva mawu,+

  • Maliko 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 koma nkhawa+ za m’nthawi* ino, chinyengo champhamvu cha chuma,+ komanso zilakolako+ za zinthu zina, zimalowa ndi kulepheretsa mawuwo kukula, ndipo sabala zipatso.+

  • Luka 8:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Zinanso zinagwera paminga. Mingazo zinali kukulira limodzi ndi mbewuzo ndipo zinalepheretsa mbewuzo kukula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena