Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 25:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndipo patebulopo uziikapo mkate wachionetsero pamaso panga nthawi zonse.+

  • Ekisodo 29:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ndipo Aroni ndi ana ake adye+ nyama ya nkhosayo ndi mkate umene uli m’dengu, adyere pakhomo la chihema chokumanako.

  • Levitiko 24:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mkatewo uzikhala wa Aroni ndi ana ake,+ ndipo aziudyera m’malo oyera,+ chifukwa wapatsidwa kwa iye monga chinthu choyera koposa kuchokera pa nsembe zotentha ndi moto zoperekedwa kwa Yehova. Limeneli likhale lamulo mpaka kalekale.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena