Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:57
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 57 Amene anagwira Yesu aja anapita naye kwa Kayafa+ mkulu wa ansembe, kumene alembi ndi akulu anali atasonkhana.+

  • Yohane 18:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choyamba anapita naye kwa Anasi, pakuti anali mpongozi wa Kayafa, amene anali mkulu wa ansembe chaka chimenecho.+

  • Yohane 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kenako Anasi anatumiza Yesu ali womangidwa kwa Kayafa mkulu wa ansembe.+

  • Machitidwe 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 (Pamenepo panalinso Anasi+ wansembe wamkulu, Kayafa,+ Yohane, Alekizanda, ndi achibale ambiri a wansembe wamkuluyo.)

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena