Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 29:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Anakhalanso ndi pakati pena n’kubereka mwana wamwamuna, ndipo anati: “Tsopano nditamanda Yehova.” Choncho Leya anatcha mwanayo, Yuda.*+ Atabereka mwana ameneyu, anayamba waleka kubereka.

  • Rute 4:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndipo kudzera mwa ana amene Yehova adzakupatsa kwa mtsikanayu,+ nyumba yako ikhale ngati nyumba ya Perezi, amene Tamara anaberekera Yuda.”+

  • 1 Mbiri 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tamara+ mpongozi wake ndiye anam’berekera Perezi+ ndi Zera. Ana onse a Yuda anali asanu.

  • Mateyu 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yuda anabereka Perezi+ ndi Zera, ndipo mayi awo anali Tamara.

      Perezi anabereka Hezironi.+

      Hezironi anabereka Ramu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena