Mateyu 9:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Koma Yesu, podziwa zimene iwo anali kuganiza,+ ananena kuti: “N’chifukwa chiyani mukuganiza zinthu zoipa m’mitima mwanu?+ Maliko 2:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Koma nthawi yomweyo Yesu anazindikira mumtima mwake kuti iwo anali kuganiza zimenezo, ndipo anawafunsa kuti: “N’chifukwa chiyani mukuganiza zimenezi m’mitima mwanu?+
4 Koma Yesu, podziwa zimene iwo anali kuganiza,+ ananena kuti: “N’chifukwa chiyani mukuganiza zinthu zoipa m’mitima mwanu?+
8 Koma nthawi yomweyo Yesu anazindikira mumtima mwake kuti iwo anali kuganiza zimenezo, ndipo anawafunsa kuti: “N’chifukwa chiyani mukuganiza zimenezi m’mitima mwanu?+