Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako ophunzira a Yohane anabwera kwa iye n’kumufunsa kuti: “N’chifukwa chiyani ife ndi Afarisi timasala kudya koma ophunzira anu sasala kudya?”+

  • Maliko 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ophunzira a Yohane ndi Afarisi anali kusala kudya. Choncho iwo anabwera kwa iye ndi kumufunsa kuti: “N’chifukwa chiyani ophunzira a Yohane ndi ophunzira a Afarisi amasala kudya, koma ophunzira anu sasala kudya?”+

  • Luka 7:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kunabwera Mwana wa munthu ndipo iye akudya ndi kumwa, koma inu mumati, ‘Taonani! Munthu wosusuka ndi wokonda kwambiri vinyo, bwenzi la okhometsa msonkho ndi ochimwa!’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena