Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Palibe amene amasokerera chigamba cha nsalu yatsopano pamalaya akunja akale. Pakuti mphamvu yonse ya chigambacho ingakoke ndi kung’amba malayawo ndipo kung’ambikako kungawonjezeke kwambiri.+

  • Maliko 2:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Palibe amene amasokerera chigamba cha nsalu yatsopano pamalaya akunja akale. Ngati wina atachita zimenezi, mphamvu yonse ya chigambacho imakoka ndi kung’amba malayawo. Chigamba chatsopanocho chimang’amba malaya akalewo, ndipo kung’ambikako kumawonjezeka kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena