Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 16:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mngelo wa Yehovayo anapitiriza kulankhula ndi mkaziyo kuti: “Taona, panopo uli ndi pakati, ndipo udzabereka mwana wamwamuna. Mwanayo udzamutche Isimaeli,+ pakuti Yehova wamva kulira kwako.+

  • Oweruza 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno tsiku lina, mngelo wa Yehova anaonekera kwa mkaziyo+ ndi kumuuza kuti: “Tamvera, panopa ndiwe wosabereka ndipo ulibe mwana. Koma udzatenga pakati ndi kubereka mwana wamwamuna.+

  • Agalatiya 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma nthawi itakwana,+ Mulungu anatumiza Mwana wake,+ amene anadzabadwa kwa mkazi+ ndipo anadzakhala pansi pa chilamulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena