Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pamenepo anayamba kulankhula mawu oipa kwa Mulungu.+

      Iwo anati: “Kodi Mulungu angathe kutipatsa chakudya m’chipululu muno?”+

  • Mateyu 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma chakumadzulo ophunzira ake anabwera kwa iye ndi kunena kuti: “Kuno n’kopanda anthu ndipo nthawi yatha, auzeni anthuwa kuti anyamuke, apite m’midzimo kuti akagule chakudya.”+

  • Maliko 6:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Tsopano kunja kunada, ndipo ophunzira ake anabwera kwa iye ndi kunena kuti: “Kuno n’kopanda anthu, ndipo nthawi yatha.+

  • Yohane 6:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno Yesu atakweza maso ake ndi kuona khamu lalikulu la anthu likubwera kwa iye, anafunsa Filipo kuti: “Kodi mitanda ya mkate yodyetsa anthu onsewa tikaigula kuti?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena